Yohane 1:40 - Buku Lopatulika40 Andrea mbale wake wa Simoni Petro anali mmodzi wa awiriwo, anamva Yohane, namtsata Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Andrea mbale wake wa Simoni Petro anali mmodzi wa awiriwo, anamva Yohane, namtsata Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Mmodzi mwa aŵiri aja amene adaamva mau a Yohane natsatira Yesu, anali Andrea, mbale wake wa Simoni Petro. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Andreya mʼbale wake wa Simoni Petro, anali mmodzi wa awiriwo amene anamva zimene Yohane ananena ndiponso amene anamutsata Yesu. Onani mutuwo |