Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 1:37 - Buku Lopatulika

37 Ndipo ophunzira awiriwo anamva iye alinkulankhula, natsata Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Ndipo ophunzira awiriwo anamva iye alinkulankhula, natsata Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Ophunzira aŵiri aja atamva mauwo, adatsatira Yesu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Ophunzira ake awiriwo atamva iye akunena izi, iwo anamutsatira Yesu.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 1:37
9 Mawu Ofanana  

Munthu akondwera ndi mayankhidwe a m'kamwa mwake; ndi mau a pa nthawi yake kodi sali abwino?


ndi okhala m'mzinda umodzi adzamuka kumzinda wina, ndi kuti, Tiyeni msanga kukapepeza Yehova, ndi kufunafuna Yehova wa makamu; ndimuka inenso.


ndipo poyang'ana Yesu alikuyenda, anati, Onani Mwanawankhosa wa Mulungu!


Koma Yesu anacheuka, napenya iwo alikumtsata, nanena nao, Mufuna chiyani? Ndipo anati kwa Iye, Rabi (ndiko kunena posandulika, Mphunzitsi), mukhala kuti?


M'mawa mwake anafuna kutuluka kunka ku Galileya, napeza Filipo. Ndipo Yesu ananena naye, Tsata Ine.


Chomwecho chikhulupiriro chidza ndi mbiri, ndi mbiri idza mwa mau a Khristu.


Nkhani yonse yovunda isatuluke m'kamwa mwanu, koma ngati pali ina yabwino kukumangirira monga mofunika ndiyo, kuti ipatse chisomo kwa iwo akumva.


Ndipo Mzimu ndi mkwatibwi anena, Idzani. Ndipo wakumva anene, Idzani. Ndipo wakumva ludzu adze; iye wofuna, atenge madzi a moyo kwaulere.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa