Yohane 1:31 - Buku Lopatulika31 Ndipo sindinamdziwe Iye; koma kuti aonetsedwe kwa Israele, chifukwa cha ichi ndinadza ine kudzabatiza ndi madzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ndipo sindinamdziwa Iye; koma kuti aonetsedwe kwa Israele, chifukwa cha ichi ndinadza ine kudzabatiza ndi madzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Inenso sindinkamudziŵa, koma ndidabwera kudzabatiza ndi madzi kuti Aisraele amdziŵe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Ine mwini sindinamudziwe Iye, koma ndinabwera kubatiza ndi madzi kuti Iye adziwike mu Israeli.” Onani mutuwo |