Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 1:24 - Buku Lopatulika

24 Ndipo otumidwawo anali a kwa Afarisi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndipo otumidwawo anali a kwa Afarisi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Anthu aja adaaŵatuma ndi Afarisi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Tsopano Afarisi ena amene anatumidwa

Onani mutuwo Koperani




Yohane 1:24
13 Mawu Ofanana  

Mfarisi iwe wakhungu, yambawatsuka m'kati mwa chikho ndi mbale, kuti kunja kwake kukhalenso koyera.


Ndipo pamene Iye anatuluka m'menemo, alembi ndi Afarisi anayamba kumuumiriza Iye kolimba, ndi kumfunsa zinthu zambiri;


Koma Afarisi, ndiwo okonda ndalama, anamva izi zonse; ndipo anamseka.


Koma Afarisi ndi achilamulo anakaniza uphungu wa Mulungu kwa iwo okha, popeza sanabatizidwe ndi iye.


Anati, Ndine mau a wofuula m'chipululu, Lungamitsani njira ya Mbuye, monga anati Yesaya mneneriyo.


Ndipo anamfunsa iye, nati kwa iye, Koma ubatiza bwanji, ngati suli Khristu, kapena Eliya, kapena Mneneriyo?


Pakutitu Asaduki anena kuti kulibe kuuka kwa akufa, kapena mngelo, kapena mzimu; koma Afarisi avomereza ponse pawiri.


andidziwa ine chiyambire, ngati afuna kuchitapo umboni, kuti ndinakhala Mfarisi monga mwa mpatuko wolunjikitsitsa wa chipembedzero chathu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa