Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 1:23 - Buku Lopatulika

23 Anati, Ndine mau a wofuula m'chipululu, Lungamitsani njira ya Mbuye, monga anati Yesaya mneneriyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Anati, Ndine mau a wofuula m'chipululu, Lungamitsani njira ya Mbuye, monga anati Yesaya mneneriyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Yohane adaŵayankha kuti, “Monga adaanenera mneneri Yesaya: “Ine ndine liwu la munthu wofuula m'chipululu; akunena kuti, ‘Ongolani mseu wodzadzeramo Ambuye.’ ”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Yohane anayankha ndi mawu a mneneri Yesaya kuti, “Ine ndi mawu a wofuwula mʼchipululu, ‘Wongolani njira ya Ambuye.’ ”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 1:23
9 Mawu Ofanana  

Pakuti uyu ndiye ananenayo Yesaya mneneri, kuti, Mau a wofuula m'chipululu, konzani khwalala la Ambuye, lungamitsani njira zake.


Mau a wofuula m'chipululu, konzani khwalala la Ambuye, lungamitsani njira zake.


Chifukwa chake anati kwa iye, Ndiwe yani? Kuti tibwezere mau kwa iwo anatituma ife. Unena chiyani za iwe wekha?


Ndipo otumidwawo anali a kwa Afarisi.


Inu nokha mundichitira umboni, kuti ndinati, Sindine Khristu, koma kuti ndili wotumidwa m'tsogolo mwake mwa Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa