Yohane 1:11 - Buku Lopatulika11 Anadza kwa zake za Iye yekha, ndipo ake a mwini yekha sanamlandire Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Anadza kwa zake za Iye yekha, ndipo ake a mwini yekha sanamlandire Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Adaabwera kwao ndithu, koma anthu ake omwe sadamlandire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Iye anabwera kwa iwo amene anali akeake, koma akewo sanamulandire Iye. Onani mutuwo |