Yeremiya 7:4 - Buku Lopatulika4 Musakhulupirire mau onama, kuti, Kachisi wa Yehova, Kachisi wa Yehova, Kachisi wa Yehova ndi awa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Musakhulupirire mau onama, kuti, Kachisi wa Yehova, Kachisi wa Yehova, Kachisi wa Yehova ndi awa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Musamangodzinyenga ndi maganizo akuti muli pabwino ponena kuti, ‘Malo ano ndi Nyumba ya Chauta, Nyumba ya Chauta, Nyumba ya Chauta!’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Musamakhulupirire mawu anu achinyengo onena kuti, ‘Ino ndi Nyumba ya Yehova, Nyumba ya Yehova, Nyumba ya Yehova!’ Onani mutuwo |