Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yeremiya 7:1 - Buku Lopatulika

1 Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Chauta adauza Yeremiya mau aŵa akuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Mawu amene Yehova anayankhula kwa Yeremiya ndi awa,

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 7:1
5 Mawu Ofanana  

Ndipo mau a Yehova anadza kwa iye, nati,


Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, nati,


Mau amene anadza kwa Yeremiya za anthu onse a Yuda chaka chachinai cha Yehoyakimu mwana wake wa Yosiya, mfumu ya Yuda; ndicho chaka choyamba cha Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni;


Anthu adzawatcha nthale ya siliva, pakuti Yehova wakana iwo.


Ima m'chipata cha nyumba ya Yehova, lalikira m'menemo mau awa, ndi kuti, Tamvani mau a Yehova, inu nonse a Yuda, amene alowa m'zipata izi kuti mugwadire Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa