Yeremiya 51:1 - Buku Lopatulika1 Yehova atero: Taonani, ndidzaukitsira Babiloni, ndi iwo okhala mu Lebi-kamai, mphepo yoononga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Yehova atero: Taonani, ndidzaukitsira Babiloni, ndi iwo okhala m'Lebi-kamai, mphepo yoononga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chauta akunena kuti, “Ndidzautsa mphepo yoti idzaononge Babiloni pamodzi ndi onse okhala m'dziko la Babiloni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yehova akuti, “Taonani, ndidzadzutsa mphepo yowononga kuti iwononge Babuloni pamodzi ndi anthu a ku Lebi Kamai. Onani mutuwo |