Yeremiya 4:8 - Buku Lopatulika8 Pamenepo, valani chiguduli, lirani ndi kubuula; pakuti mkwiyo wa kuopsa wa Yehova sunabwerere pa ife. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Pamenepo, valani chiguduli, lirani ndi kubuula; pakuti mkwiyo wa kuopsa wa Yehova sunabwerera pa ife. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Motero valani ziguduli, mudandaule ndi kulira kwambiri. Pakuti mkwiyo woopsa wa Chauta sudatichoke.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Choncho valani ziguduli, lirani ndi kubuwula, pakuti mkwiyo waukulu wa Yehova sunatichokere. Onani mutuwo |