Yeremiya 4:12 - Buku Lopatulika12 mphepo yolimba yochokera kumeneko idzandifika ine; tsopanonso ndidzaweruza iwo maweruzo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 mphepo yolimba yochokera kumeneko idzandifika ine; tsopanonso ndidzaweruza iwo maweruzo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Imeneyo ndi mphepo yamphamvu zedi yochokera kwa Ine Mulungu. Ndipo ndi Ineyo amene ndikuŵaimba mlandu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 koma mphepo yamphamvu kwambiri yochokera kwa Ine. Tsono ndi Ineyo amene ndikuwaweruza.” Onani mutuwo |