Yeremiya 4:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo ndinati, Ha, Yehova Mulungu! Ndithu mwanyenga kwambiri anthu awa ndi Yerusalemu, ndi kuti, Mudzalandira mtendere; koma lupanga lafikira pamoyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo ndinati, Ha, Yehova Mulungu! Ndithu mwanyenga kwambiri anthu awa ndi Yerusalemu, ndi kuti, Mudzalandira mtendere; koma lupanga lafikira pamoyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Tsono ndidati, “Ha, Ambuye Chauta, ndithu mudaŵanyenga anthu aŵa pamodzi ndi a mu Yerusalemu! Mudaŵauza kuti, ‘Mudzakhala pa mtendere,’ koma chonsecho lupanga lili pamutu pao.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndipo ine ndinati, “Haa, Ambuye Yehova, ndithu munawanyenga anthu awa pamodzi ndi Yerusalemu pamene munanena kuti, ‘Mudzakhala pa mtendere,’ chonsecho lupanga lili pakhosi pathu.” Onani mutuwo |