Yeremiya 32:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo ndinagula mundawo wa ku Anatoti kwa Hanamele mwana wa mbale wa atate wanga, ndimyesera ndalama, masekeli khumi ndi asanu ndi awiri a siliva. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo ndinagula mundawo wa ku Anatoti kwa Hanamele mwana wa mbale wa atate wanga, ndimyesera ndalama, masekeli khumi ndi asanu ndi awiri a siliva. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Motero ndidagula mundawo ku Anatoti kwa Hanamele msuweni wanga, ndipo mtengo wake unali masekeli asiliva 17. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 choncho ndinagula munda wa ku Anatoti kwa Hanameli msuweni wanga, ndipo ndinamupatsa masekeli asiliva 17. Onani mutuwo |