Yeremiya 32:2 - Buku Lopatulika2 Nthawi yomweyo nkhondo ya mfumu ya Babiloni inamangira Yerusalemu misasa; ndipo Yeremiya mneneri anatsekeredwa m'bwalo la kaidi, linali kunyumba ya mfumu ya Yuda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Nthawi yomweyo nkhondo ya mfumu ya Babiloni inamangira Yerusalemu misasa; ndipo Yeremiya mneneri anatsekeredwa m'bwalo la kaidi, linali kunyumba ya mfumu ya Yuda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pa nthaŵi imeneyo ankhondo a mfumu ya ku Babiloni ankazinga Yerusalemu ndi zithando zankhondo. Mneneri Yeremiya anali atamtsekera m'bwalo la alonda, m'kati mwa nyumba yaufumu ya ku Yuda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Pa nthawi imeneyi nʼkuti ankhondo a mfumu ya ku Babuloni atazinga Yerusalemu, ndipo mneneri Yeremiya ndiye anamutsekera mʼbwalo la alonda mʼnyumba yaufumu ya ku Yuda. Onani mutuwo |