Yeremiya 26:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo iwe uziti kwa iwo, Yehova atero: Ngati simudzandimvera Ine kuyenda m'chilamulo changa, chimene ndachiika pamaso panu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo iwe uziti kwa iwo, Yehova atero: Ngati simudzandimvera Ine kuyenda m'chilamulo changa, chimene ndachiika pamaso panu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ukaŵauze kuti, Chauta akuti: Ngati simundimvera Ine, ngati simutsata malamulo amene ndidakupatsani, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ukawawuze kuti, ‘Yehova akuti: Ngati simundimvera Ine ndi kuleka kutsatira malamulo anga, amene ndakupatsani, Onani mutuwo |