Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yeremiya 22:1 - Buku Lopatulika

1 Yehova atero: Tsikira kunyumba ya mfumu ya Yuda, ndi kunena komweko mau awa,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Yehova atero: Tsikira kunyumba ya mfumu ya Yuda, ndi kunena komweko mau awa,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Chauta adandiwuza kuti, “Pita ku nyumba ya mfumu ya ku Yuda, ukaiwuze kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Yehova anandiwuza kuti, “Pita ku nyumba ya mfumu ya ku Yuda ndipo ukayiwuze kuti,

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 22:1
15 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anatumiza Natani kwa Davide. Ndipo anafika kwa iye nanena naye, Mu mzinda wina munali anthu awiri; wina wolemera, wina wosauka.


Ndipo Yehova analankhula ndi Manase ndi anthu ake, koma sanasamalire.


Ndipo za nyumba ya mfumu ya Yuda, tamvani mau a Yehova:


Ndipo ndidzakulangani inu monga mwa chipatso cha ntchito zanu, ati Yehova; ndipo ndidzayatsa moto m'nkhalango mwake, ndipo udzatha zonse zomzungulira iye.


ndi kuti, Tamvani mau a Yehova, Inu mfumu ya Yuda, amene mukhala pa mpando wa Davide, inu, ndi atumiki anu, ndi anthu anu amene alowa pa zipata izi.


Yehova Mulungu wa Israele atero, Pita, nena kwa Zedekiya mfumu ya Yuda, numuuze iye, kuti Yehova atero, Taona, ndidzapereka mzindawu m'dzanja la mfumu ya ku Babiloni, ndipo adzautentha ndi moto;


Imvani ichi, ansembe inu; mverani, inu nyumba ya Israele; tcherani khutu, inu nyumba ya mfumu; pakuti chiweruzochi chinena inu; pakuti munakhala msampha ku Mizipa, ndi ukonde woyalidwa pa Tabori.


koma usaneneranso ku Betele; pakuti pamenepo mpamalo opatulika a mfumu, ndiyo nyumba yachifumu.


Pakuti Yohane adanena kwa Herode, Si kuloledwa kwa inu kukhala naye mkazi wa mbale wanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa