Yeremiya 22:1 - Buku Lopatulika1 Yehova atero: Tsikira kunyumba ya mfumu ya Yuda, ndi kunena komweko mau awa, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Yehova atero: Tsikira kunyumba ya mfumu ya Yuda, ndi kunena komweko mau awa, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chauta adandiwuza kuti, “Pita ku nyumba ya mfumu ya ku Yuda, ukaiwuze kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yehova anandiwuza kuti, “Pita ku nyumba ya mfumu ya ku Yuda ndipo ukayiwuze kuti, Onani mutuwo |