Yeremiya 15:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Yehova anati kwa ine, Ngakhale Mose ndi Samuele akadaima pamaso panga, koma mtima wanga sukadasamalira anthu awa; muwachotse iwo pamaso panga, atuluke. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Yehova anati kwa ine, Ngakhale Mose ndi Samuele akadaima pamaso panga, koma mtima wanga sukadasamalira anthu awa; muwachotse iwo pamaso panga, atuluke. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pambuyo pake Chauta adandiwuza kuti, “Ngakhale Mose ndi Samuele akadaima pamaso panga akupempherera anthu ameneŵa, sindikadaŵamvera chisoni. Achotseni, ndisaŵaonenso, apite basi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Kenaka Yehova anandiwuza kuti, “Ngakhale Mose ndi Samueli akanayima pamaso panga kupempherera anthu awa, Ine sindikanawachitira chisoni. Achotseni ndipo ndisawaonenso! Aleke apite! Onani mutuwo |