Yeremiya 15:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo padzakhala, pamene adzati kwa iwe, Titulukire kuti? Pamenepo uziti, Atero Yehova: Amene a kuimfa, anke kuimfa; amene a kulupanga, anke kulupanga; amene a kunjala, anke kunjala; ndi amene a kunsinga, anke kunsinga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo padzakhala, pamene adzati kwa iwe, Titulukire kuti? Pamenepo uziti, Atero Yehova: Amene a kuimfa, anke kuimfa; amene a kulupanga, anke kulupanga; amene a kunjala, anke kunjala; ndi amene a kunsinga, anke kunsinga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Akakufunsa kuti, ‘Kodi tipite kuti?’ Uŵauze kuti Ine ndati, “ ‘Oyenera mliri adzafa ndi mliri, oyenera lupanga adzafa ndi lupanga, oyenera njala adzafa ndi njala, oyenera ukapolo, adzapita ku ukapolo.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndipo ngati akufunsa iwe kuti, ‘Kodi tipite kuti?’ uwawuze kuti, ‘Yehova akuti, “ ‘Oyenera kufa adzafa; oyenera kufa ndi lupanga adzafa ndi lupanga; oyenera kufa ndi njala adzafa ndi njala; oyenera kupita ku ukapolo adzapita ku ukapolo.’ Onani mutuwo |