Yeremiya 13:9 - Buku Lopatulika9 Yehova atero, Momwemo ndidzaononga kudzitama kwa Yuda, ndi kudzitama kwakukulu kwa Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Yehova atero, Momwemo ndidzaononga kudzitama kwa Yuda, ndi kudzitama kwakukulu kwa Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Chauta adandiwuza kuti, “Ndimotu m'mene ndidzaonongere zimene a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu amanyadira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Izi ndi zimene ine ndikunena: ‘Umu ndi mmene ndidzawonongere zimene akunyadira kwambiri a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu. Onani mutuwo |