Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yeremiya 13:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Apo mau a adandifikanso:

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Pamenepo Yehova anandiwuza kuti,

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 13:8
4 Mawu Ofanana  

Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine nthawi yachiwiri, kuti,


Ndipo ndinanka ku Yufurate, ndikukumba, nditenga mpango m'malo m'mene ndinaubisamo; ndipo, taonani, mpango unaonongeka, wosayenera kanthu.


Yehova atero, Momwemo ndidzaononga kudzitama kwa Yuda, ndi kudzitama kwakukulu kwa Yerusalemu.


Ndipo ndinapenya, ndipo taonani, kuthambo lokhala pamwamba pa mitu ya akerubi kudaoneka ngati mwala wasafiro, ngati maonekedwe a chifaniziro cha mpando wachifumu pamwamba pao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa