Yeremiya 12:4 - Buku Lopatulika4 Dziko lidzalira masiku angati, nilifota therere la minda yonse? Chifukwa cha zoipa za iwo okhalamo, zithedwa zinyama, ndi mbalame; pakuti iwo anati, Iye sadzaona chitsiriziro chathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Dziko lidzalira masiku angati, nilifota therere la minda yonse? Chifukwa cha zoipa za iwo okhalamo, zithedwa zinyama, ndi mbalame; pakuti iwo anati, Iye sadzaona chitsiriziro chathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Kodi dziko lidzakhala likulirabe mpaka liti? Ndipo udzu wake udzakhalabe wouma mpaka liti? Palibe mbalame kapena nyama zimene zatsala chifukwa anthu okhalamo ndi oipa kwambiri. Amati, “Mulungu sadzaona zimene zidzatiwonekere masiku athu otsiriza.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Kodi dziko lidzakhala likulirabe mpaka liti ndipo udzu mʼmunda uliwonse udzakhalabe ofota mpaka liti? Nyama ndi mbalame kulibiretu chifukwa anthu amene amakhalamo ndi oyipa. Iwo amati: “Yehova sangathe kuona ntchito zathu.” Onani mutuwo |