Yeremiya 12:5 - Buku Lopatulika5 Ngati wathamanga pamodzi ndi oyenda pansi, ndipo iwo anakulemetsa iwe, udzayesana nao akavalo bwanji? Ndipo ngakhale ukhazikika m'dziko lamtendere, udzachita chiyani m'kudzikuza kwa Yordani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ngati wathamanga pamodzi ndi oyenda pansi, ndipo iwo anakulemetsa iwe, udzayesana nao akavalo bwanji? Ndipo ngakhale ukhazikika m'dziko lamtendere, udzachita chiyani m'kudzikuza kwa Yordani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Chauta adayankha kuti, “Ngati kukutopetsa kuthamanga ndi anthu, nanga udzapikisana bwanji ndi akavalo? Ngati mtima wako ulefuka m'dziko lokoma, nanga udzatani m'nkhalango ya ku Yordani? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Yehova anayankha kuti, “Ngati kukutopetsa kuthamanga pamodzi ndi anthu nanga ungapikisane bwanji ndi akavalo? Ngati ukupunthwa ndi kugwa pa malo abwino, udzatha bwanji kuthamanga mʼnkhalango za ku Yorodani? Onani mutuwo |