Yeremiya 11:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo Yehova anati kwa ine, Chiwembu chaoneka mwa anthu a Yuda, ndi mwa anthu okhala mu Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo Yehova anati kwa ine, Chiwembu chaoneka mwa anthu a Yuda, ndi mwa anthu okhala m'Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Kenaka Chauta adandiwuza kuti, “Anthu a ku Yuda ndi anthu a mu Yerusalemu andiwukira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Kenaka Yehova anandiwuza kuti, “Anthu a ku Yuda ndi ku Yerusalemu andiwukira. Onani mutuwo |