Yeremiya 11:3 - Buku Lopatulika3 ndi kunena kwa iwo, Atero Yehova, Mulungu wa Aisraele: Wotembereredwa ndi munthu wosamvera mau a pangano ili, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 ndi kunena kwa iwo, Atero Yehova, Mulungu wa Aisraele: Wotembereredwa ndi munthu wosamvera mau a pangano ili, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Uŵauze kuti mau a Chauta, Mulungu wa Israele, ndi aŵa: Atembereredwe munthu amene sasunga mau a chipangano, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Awuze kuti Yehova, Mulungu wa Israeli akuti ‘adzakhala wotembereredwa munthu amene samvera mawu a pangano ili. Onani mutuwo |