Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yeremiya 11:1 - Buku Lopatulika

1 Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Mau amene anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Chauta adauza Yeremiya kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Yehova anayankhula ndi Yeremiya kuti,

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 11:1
3 Mawu Ofanana  

Ndipo mau a Yehova anadza kwa iye, nati,


Tsanulirani ukali wanu pa amitundu osakudziwani Inu, ndi pa mabanja osaitana dzina lanu; pakuti anadya Yakobo, inde, anamudya namutha, napasula mokhalamo mwake.


Imvani mau a pangano ili, nenani kwa anthu a Yuda, ndi anthu a Yerusalemu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa