Yeremiya 10:8 - Buku Lopatulika8 Koma onse pamodzi apulukira ndi kupusa; mtengo ndiwo chilangizo, chopanda pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Koma onse pamodzi apulukira ndi kupusa; mtengo ndiwo chilangizo, chopanda pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Onsewo ndi opusa ndi opanda nzeru. Nzeru zao amaphunzira ku mafano achabechabe opanga ndi mitengo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Onsewo ndi opusa ndi opanda nzeru; malangizo awo amawatenga kuchokera kwa mafano achabechabe opanga ndi mitengo. Onani mutuwo |