Yakobo 5:9 - Buku Lopatulika9 Musaipidwe wina ndi mnzake, abale, kuti mungaweruzidwe. Taonani, woweruza aima pakhomo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Musaipidwe wina ndi mnzake, abale, kuti mungaweruzidwe. Taonani, woweruza aima pakhomo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Abale musamanenerana zoipa pakati panu, kuwopa kuti Mulungu angakuweruzeni. Onani, woweruza waima pa khomo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Abale, musamanenezane zoyipa kuopa kuti mungadzaweruzidwe. Woweruza ali pa khomo! Onani mutuwo |