Yakobo 5:8 - Buku Lopatulika8 Lezani mtima inunso, limbitsani mitima yanu; pakuti kudza kwake kwa Ambuye kuyandikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Lezani mtima inunso, limbitsani mitima yanu; pakuti kudza kwake kwa Ambuye kuyandikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Inunso khazikani mtima. Limbani mtima, pakuti Ambuye ali pafupi kubwera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Inunso mukhale owugwira mtima ndi osasinthika chifukwa Ambuye ali pafupi kubwera. Onani mutuwo |