Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yakobo 5:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo anapempheranso; ndipo m'mwamba munatsika mvula, ndi dziko lidabala zipatso zake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo anapempheranso; ndipo m'mwamba munatsika mvula, ndi dziko lidabala zipatso zake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Atapempheranso, mvula idagwa, nthaka nkuyambanso kumeretsa mbeu zake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Kenaka anapempheranso, ndipo kumwamba kunagwetsa mvula, ndipo dziko lapansi linatulutsa zomera zake.

Onani mutuwo Koperani




Yakobo 5:18
4 Mawu Ofanana  

Nati iye, Sindimavute Israele ine ai, koma inu ndi nyumba ya atate wanu; popeza munasiya malamulo a Yehova, ndi kutsata Abaala.


Mwa zachabe za mitundu ya anthu zilipo kodi, zimene zingathe kuvumbitsa mvula? Kapena miyamba kubweretsa mivumbi? Kodi si ndinu, Yehova, Mulungu wathu? Ndipo tidzakudikirani Inu; pakuti munalenga zonse zimenezi.


Koma sanadzisiyire Iye mwini wopanda umboni, popeza anachita zabwino, nakupatsani inu zochokera kumwamba mvula ndi nyengo za zipatso, ndi kudzaza mitima yanu ndi chakudya ndi chikondwero.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa