Yakobo 5:19 - Buku Lopatulika19 Abale anga, ngati wina wa inu asochera posiyana ndi choonadi, ndipo ambweza iye mnzake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Abale anga, ngati wina wa inu asochera posiyana ndi choonadi, ndipo ambweza iye mnzake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Abale anga, wina mwa inu akasokera pa kusiya choona, mnzake nkumubweza, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Abale anga, ngati mmodzi wa inu apatuka pa choonadi ndipo wina wake ndi kumubweza, Onani mutuwo |