Yakobo 5:13 - Buku Lopatulika13 Kodi wina wa inu akumva zowawa? Apemphere. Kodi wina asekera? Aimbire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Kodi wina wa inu akumva zowawa? Apemphere. Kodi wina asekera? Aimbire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Kodi wina mwa inu ali m'mavuto? Apemphere. Kodi wina wakondwa? Aimbe nyimbo zotamanda Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Kodi alipo wina mwa inu amene ali pa mavuto? Apemphere. Kodi wina wakondwa? Ayimbe nyimbo zolemekeza. Onani mutuwo |