Yakobo 4:9 - Buku Lopatulika9 Khalani osautsidwa, lirani, lirani misozi; kuseka kwanu kusanduke kulira, ndi chimwemwe chanu chisanduke chisoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Khalani osautsidwa, lirani, lirani misozi; kuseka kwanu kusanduke kulira, ndi chimwemwe chanu chisanduke chisoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Zindikirani umphaŵi wanu, imvani chisoni, lirani misozi. Kuseka kwanu kusanduke kulira, ndipo chimwemwe chanu chisanduke chisoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Chitani chisoni chifukwa cha zimene mwachita, lirani misozi. Kuseka kwanu kusanduke kulira, ndipo chimwemwe chanu chisanduke chisoni. Onani mutuwo |