Yakobo 3:8 - Buku Lopatulika8 koma lilime palibe munthu akhoza kulizoloweretsa; lili choipa chotakataka, lodzala ndi ululu wakupha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 koma lilime palibe munthu akhoza kulizoloweretsa; lili choipa chotakataka, lodzala ndi ululu wakupha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Koma lilime palibe munthu amene angathe kuliŵeta. Ndi loipa, silidziŵa kupumula, ndipo ndi lodzaza ndi ululu wakupha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 koma palibe munthu amene angaweta lilime. Lilime ndipo silitha kupuma, ndi lodzaza ndi ululu wakupha. Onani mutuwo |