Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yakobo 3:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo chipatso cha chilungamo chifesedwa mumtendere kwa iwo akuchita mtendere.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo chipatso cha chilungamo chifesedwa mumtendere kwa iwo akuchita mtendere.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Ndipo chilungamo ndiye chipatso cha mbeu zimene anthu odzetsa mtendere amafesa mu mtendere.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Anthu amtendere amene amadzala mtendere amakolola chilungamo.

Onani mutuwo Koperani




Yakobo 3:18
13 Mawu Ofanana  

Atakalamba adzapatsanso zipatso; adzadzazidwa ndi madzi nadzakhala abiriwiri,


Woipa alandira malipiro onyenga; koma wofesa chilungamo aonadi mphotho.


Wokhulupirira chuma chake adzagwa; koma olungama adzaphuka ngati tsamba.


Chipatso cha wolungama ndi mtengo wa moyo; ndipo wokola mtima ali wanzeru.


Mudzibzalire m'chilungamo mukolole monga mwa chifundo; limani masala anu, pakuti yafika nthawi ya kufuna Yehova, mpaka afika Iye, navumbitsira inu chilungamo.


Kodi akavalo adzathamanga pathanthwe? Kodi adzalimako ndi ng'ombe pakuti mwasanduliza chiweruzo chikhale ndulu, ndi chipatso cha chilungamo chikhale chivumulo;


Odala ali akuchita mtendere; chifukwa adzatchedwa ana a Mulungu.


Wakumweta alandira kulipira, nasonkhanitsira chobala kumoyo wosatha; kuti wofesayo akakondwere pamodzi ndi womwetayo.


Pakuti wakufesera kwa thupi la iye yekha, chochokera m'thupi adzatuta chivundi; koma wakufesera kwa Mzimu, chochokera mu Mzimu adzatuta moyo wosatha.


odzala nacho chipatso cha chilungamo, chimene chili mwa Yesu Khristu, kuchitira Mulungu ulemerero ndi chiyamiko.


Chilango chilichonse, pakuchitika, sichimveka chokondweretsa, komatu chowawa; koma chitatha, chipereka chipatso cha mtendere, kwa iwo ozoloweretsedwa nacho, ndicho cha chilungamo.


Pakuti mkwiyo wa munthu suchita chilungamo cha Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa