Yakobo 3:16 - Buku Lopatulika16 Pakuti pomwe pali kaduka ndi zotetana, pamenepo pali chisokonekero ndi chochita choipa chilichonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Pakuti pomwe pali kaduka ndi zotetana, pamenepo pali chisokonekero ndi chochita choipa chilichonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Pajatu pamene pali kaduka ndi kudzikonda, pomweponso pali chisokonezo ndi ntchito yoipa ya mtundu uliwonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Pakuti pamene pali kaduka ndi kudzikonda pomweponso pamakhala chisokonezo ndi zochitika zoyipa zonse. Onani mutuwo |