Yakobo 3:15 - Buku Lopatulika15 Nzeru iyi, sindiyo yotsika kumwamba, komatu ili ya padziko, ya chifuniro cha chibadwidwe, ya ziwanda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Nzeru iyi, sindiyo yotsika kumwamba, komatu ili ya padziko, ya chifuniro cha chibadwidwe, ya ziwanda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Nzeru zotere si zochokera Kumwamba, koma ndi nzapansipano, ndi za anthu chabe, ndiponso nzochokera ku mizimu yoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 “Nzeru” zotere sizochokera kumwamba koma ndi za mʼdziko lapansi, si zauzimu koma ndi za ziwanda. Onani mutuwo |