Yakobo 3:11 - Buku Lopatulika11 Kodi kasupe atulutsira pa uno womwewo madzi okoma ndi owawa? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Kodi kasupe atulutsira pa uno womwewo madzi okoma ndi owawa? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Kodi kasupe amatulutsa madzi omweka ndi oŵaŵa pa dzenje limodzimodzi? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Kodi madzi abwino ndi a mchere angatuluke pa kasupe mmodzi? Onani mutuwo |