Yakobo 1:2 - Buku Lopatulika2 Muchiyese chimwemwe chokha, abale anga, m'mene mukugwa m'mayesero a mitundumitundu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Muchiyese chimwemwe chokha, abale anga, m'mene mukugwa m'mayesero a mitundumitundu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Abale anga, muzikondwa ndithu mukamayesedwa ndi mavuto amitundumitundu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Abale, muchiyese ngati chimwemwe chenicheni nthawi zonse pamene mukukumana ndi mayesero amitundumitundu. Onani mutuwo |