Yakobo 1:1 - Buku Lopatulika1 Yakobo, kapolo wa Mulungu ndi wa Ambuye Yesu Khristu, kwa mafuko khumi ndi awiri a m'chibalaliko: ndikupatsani moni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Yakobo, kapolo wa Mulungu ndi wa Ambuye Yesu Khristu, kwa mafuko khumi ndi awiri a m'chibalaliko: ndikupatsani moni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ndine, Yakobe, mtumiki wa Mulungu ndi wa Ambuye Yesu Khristu. Ndikupereka moni kwa inu anthu a Mulungu, a mafuko khumi ndi aŵiri, obalalikana ku maiko osiyanasiyana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yakobo, mtumiki wa Mulungu ndi wa Ambuye Yesu Khristu, kulembera mafuko khumi ndi awiri obalalikana ku mayiko osiyanasiyana. Landirani moni. Onani mutuwo |