Tito 3:11 - Buku Lopatulika11 podziwa kuti wotereyo wasandulika konse, nachimwa, nakhala wodzitsutsa yekha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 podziwa kuti wotereyo wasandulika konse, nachimwa, nakhala wodzitsutsa yekha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Paja ukudziŵa kuti munthu wotere ngwosokonezeka ndipo ngwochimwa. Mwini wake yemwe amadziimba mlandu yekha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Iwe udziwe kuti munthu wotero ngosokoneza ndi wochimwa, ndipo akudzitsutsa yekha. Onani mutuwo |