Rute 3:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo kunali, pakati pa usiku munthuyo anadzidzimuka, natembenuka; ndipo taona pa mapazi ake pagona mkazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo kunali, pakati pa usiku munthuyo anadzidzimuka, natembenuka; ndipo taona pa mapazi ake pagona mkazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tsono pakati pa usiku Bowazi adadzidzimuka natembenuka, naona mkazi atagona ku mapazi ake. Adafunsa kuti, “Ndiwe yani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Tsono pakati pa usiku Bowazi anadzidzimuka, natembenuka, ndipo anangoona mkazi akugona ku mapazi ake. Onani mutuwo |