Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Rute 1:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo Elimeleki mwamuna wake wa Naomi anamwalira; natsala iye ndi ana ake awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo Elimeleki mwamuna wake wa Naomi anamwalira; natsala iye ndi ana ake awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Tsono Elimeleki mwamuna wa Naomi adamwalira, ndipo Naomiyo adatsala ndi ana aŵiri aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Kenaka Elimeleki, mwamuna wake wa Naomi anamwalira ndipo Naomiyo anatsala ndi ana ake aamuna awiri aja.

Onani mutuwo Koperani




Rute 1:3
6 Mawu Ofanana  

Ndipo wina wa akazi a ana a aneneri anafuula kwa Elisa, ndi kuti, Mnyamata wanu, mwamuna wanga wafa; mudziwa kuti mnyamata wanu anaopa Yehova; ndipo wafika wamangawa kunditengera ana anga awiri akhale akapolo ake.


Masautso a wolungama mtima achuluka, koma Yehova amlanditsa mwa onsewa.


pakuti iye amene Ambuye amkonda amlanga, nakwapula mwana aliyense amlandira.


Dzina la munthuyo ndiye Elimeleki, ndi dzina la mkazi wake ndiye Naomi, ndi maina a ana ake awiri ndiwo Maloni, ndi Kilioni; ndiwo Aefurati a ku Betelehemu ku Yuda. Iwowa ndipo analowa m'dziko la Mowabu, nakhala komweko.


Nadzitengera iwo akazi a ku Mowabu; wina dzina lake ndiye Oripa, mnzake dzina lake ndiye Rute; ndipo anagonera komweko ngati zaka khumi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa