Rute 1:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Elimeleki mwamuna wake wa Naomi anamwalira; natsala iye ndi ana ake awiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Elimeleki mwamuna wake wa Naomi anamwalira; natsala iye ndi ana ake awiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono Elimeleki mwamuna wa Naomi adamwalira, ndipo Naomiyo adatsala ndi ana aŵiri aja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kenaka Elimeleki, mwamuna wake wa Naomi anamwalira ndipo Naomiyo anatsala ndi ana ake aamuna awiri aja. Onani mutuwo |