Obadiya 1:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo usaime pamphambano kuononga opulumuka ake; kapena kupereka otsala ake tsiku lakupsinjika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo usaime pamphambano kuononga opulumuka ake; kapena kupereka otsala ake tsiku lakupsinjika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Simukadayenera kudikira pa mphambano za miseu kuti mugwire anthu othaŵa. Pa tsiku lao la tsoka simukadayenera kupereka anthu ao otsala kwa adani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Sunayenera kudikirira pamphambano ya misewu kuti uphe Ayuda othawa, kapena kuwapereka kwa adani awo Ayuda opulumuka pa nthawi ya mavuto awo.” Onani mutuwo |