Numeri 8:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Alevi aike manja ao pa mitu ya ng'ombezo; pamenepo ukonze imodzi ikhale nsembe yauchimo, ndi inzake, nsembe yopsereza za Yehova, kuchita chotetezera Alevi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Alevi aike manja ao pa mitu ya ng'ombezo; pamenepo ukonze imodzi ikhale nsembe yauchimo, ndi inzake, nsembe yopsereza za Yehova, kuchita chotetezera Alevi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Pambuyo pake Alevi asanjike manja ao pamitu ya ng'ombe zamphongo, ndipo iwe upereke kwa Chauta ng'ombe imodzi kuti ikhale nsembe yopepesera machimo. Inayo uipereke kuti ikhale nsembe yopsereza, kuchitira mwambo wopepesera machimo a Alevi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 “Alevi akatsiriza kusanjika manja awo pa mitu ya ngʼombe zazimuna, imodzi ikhale ya nsembe yopepesera machimo ndipo inayo ikhale ya nsembe yopsereza ya kwa Yehova, kupepesera machimo a Alevi. Onani mutuwo |