Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 7:77 - Buku Lopatulika

77 ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ndicho chopereka cha Pagiyele mwana wa Okarani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

77 ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ndicho chopereka cha Pagiyele mwana wa Okarani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

77 Ndipo zoperekera nsembe yachiyanjano zinali ng'ombe ziŵiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, ndi anaankhosa asanu amphongo a chaka chimodzi. Zimenezi ndizo zimene zinali zopereka za Pagiyele mwana wa Okarani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

77 ngʼombe ziwiri zazimuna, nkhosa zazimuna zisanu, mbuzi zazimuna zisanu, ndi ana ankhosa aamuna asanu a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Pagieli mwana wa Okirani.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 7:77
4 Mawu Ofanana  

Wa Asere, Pagiyele mwana wa Okarani.


Ndipo iwo akumanga mahema ao poyandikizana naye ndiwo a fuko la Asere; ndi kalonga wa ana a Asere ndiye Pagiyele mwana wa Okarani.


tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo;


Tsiku lakhumi ndi chiwiri kalonga wa ana a Nafutali, ndiye Ahira mwana wa Enani:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa