Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 7:59 - Buku Lopatulika

59 ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ndicho chopereka cha Gamaliele mwana wa Pedazuri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

59 ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ndicho chopereka cha Gamaliele mwana wa Pedazuri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

59 Ndipo zoperekera nsembe yachiyanjano zinali ng'ombe ziŵiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, ndi anaankhosa asanu amphongo a chaka chimodzi. Zimenezi ndizo zimene zinali zopereka za Gamaliele mwana wa Pedazuri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

59 ngʼombe zazimuna ziwiri, nkhosa zazimuna zisanu, mbuzi zazimuna zisanu ndi ana ankhosa a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Gamalieli mwana wa Pedazuri.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 7:59
3 Mawu Ofanana  

Ndipo chopereka chake chikakhala nsembe yoyamika; akabwera nayo ng'ombe, kapena yaimuna kapena yaikazi, azibwera nayo yopanda chilema pamaso pa Yehova.


Ndipo oyandikizana naye ndiwo a fuko la Manase; ndi kalonga wa ana a Manase ndiye Gamaliele mwana wa Pedazuri.


tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa