Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 5:20 - Buku Lopatulika

20 Koma iwe, ngati wapatukira mwamuna wako, ngati wadetsedwa, kuti wagona nawe munthu, wosati mwamuna wako;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Koma iwe, ngati wapatukira mwamuna wako, ngati wadetsedwa, kuti wagona nawe munthu, wosati mwamuna wako;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Koma ngati udamzemberapo mwamuna wako, ngakhale kuti unali m'manja mwake, nudziipitsa, ndipo ngati udagona ndi mwamuna wina wosakhala mwamuna wako,’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Koma ngati wayenda njira yoyipa uli pa ukwati ndi mwamuna wako ndi kudzidetsa pogonana ndi mwamuna amene si mwamuna wako,’

Onani mutuwo Koperani




Numeri 5:20
2 Mawu Ofanana  

Ndipo munthu aliyense akagona uipa, azisamba thupi lake lonse ndi madzi, nadzakhala wodetsedwa kufikira madzulo.


Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Mkazi wamwini akapatukira mwamuna wake, nakamchitira mosakhulupirika,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa