Numeri 5:12 - Buku Lopatulika12 Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Mkazi wamwini akapatukira mwamuna wake, nakamchitira mosakhulupirika, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Mkazi wa mwini akapatukira mwamuna wake, nakamchitira mosakhulupirika, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 “Uza Aisraele kuti, mwina mkazi adzazembera mwamuna wake namachita zosakhulupirika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 “Yankhula ndi Aisraeli ndipo uwawuze kuti, ‘Ngati mkazi wa munthu wina ayenda njira yosayenera nakhala wosakhulupirika kwa mwamuna wake, Onani mutuwo |