Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 5:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 “Yankhula ndi Aisraeli ndipo uwawuze kuti, ‘Ngati mkazi wa munthu wina ayenda njira yosayenera nakhala wosakhulupirika kwa mwamuna wake,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

12 Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Mkazi wamwini akapatukira mwamuna wake, nakamchitira mosakhulupirika,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Mkazi wa mwini akapatukira mwamuna wake, nakamchitira mosakhulupirika,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 “Uza Aisraele kuti, mwina mkazi adzazembera mwamuna wake namachita zosakhulupirika.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 5:12
6 Mawu Ofanana  

“Usachite chigololo.


Kenaka Yehova anawuza Mose kuti,


“ ‘Limeneli ndiye lamulo la nsanje pamene mkazi wayenda njira yoyipa ndi kudzidetsa ali pa ukwati ndi mwamuna wake,


Ngati mwamuna wakwatira mkazi amene sakukondwera naye chifukwa wapeza vuto pa mkaziyo, namulembera mkaziyo kalata ya chisudzulo, namupatsa ndi kumutulutsa mʼnyumba mwake,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa