Numeri 34:5 - Buku Lopatulika5 ndipo malirewo adzapinda ku Azimoni kunka ku mtsinje wa Ejipito, ndi kutuluka kwao adzatuluka kunyanja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 ndipo malirewo adzapinda ku Azimoni kunka ku mtsinje wa Ejipito, ndi kutuluka kwao adzatuluka kunyanja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Malirewo akhotere ku Azimoni ndi kumapita ku mtsinje wa ku Ejipito, ndipo akathere ku Nyanja.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 kumene malirewo adzakhote kuchokera ku Azimoni mpaka ku khwawa la ku Igupto ndi kukathera ku Nyanja Yayikulu. Onani mutuwo |